Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 43:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Tumizani kuwala kwanu ndi choonadi chanu.+

      Zimenezi zinditsogolere.+

      Zinditsogolere kuphiri lanu lopatulika ndi kuchihema chanu chachikulu.+

  • Miyambo 6:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Chifukwa lamulolo ndi nyale,+

      Ndipo malangizo ndi kuwala,+

      Komanso kudzudzula kumene kumathandiza munthu kusintha ndi njira yakumoyo.+

  • Yesaya 51:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Inu anthu anga, ndimvereni.

      Iwe mtundu wanga,+ tchera khutu kwa ine.

      Chifukwa kwa ine kudzachokera lamulo+

      Ndipo ndidzachititsa kuti chilungamo changa chikhazikike ngati kuwala ku mitundu ya anthu.+

  • Aroma 15:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Zinthu zonse zimene zinalembedwa kalekale zinalembedwa kuti zitilangize.+ Malembawa amatithandiza kupirira+ ndiponso amatilimbikitsa nʼcholinga choti tikhale ndi chiyembekezo.+

  • 2 Timoteyo 3:16, 17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Malemba onse anauziridwa ndi Mulungu,+ ndipo ndi othandiza pophunzitsa,+ kudzudzula, kukonza zinthu ndi kulangiza mwachilungamo,+ 17 kuti munthu wa Mulungu akhale woyenerera kwambiri ndi wokonzeka mokwanira kugwira ntchito iliyonse yabwino.

  • 2 Petulo 1:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Nʼchifukwa chake sitikayikira ngakhale pangʼono kuti mawu aulosiwa adzakwaniritsidwa ndipo mukuchita bwino kuwaganizira mozama. Mawu amenewa aziwala mʼmitima yanu ngati nyale+ imene ikuwala mumdima. Pitirizani kuchita zimenezi mpaka mʼbandakucha, nthanda*+ itatuluka.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena