Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 33:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Wosangalala ndi mtundu umene Mulungu wawo ndi Yehova,+

      Anthu amene iye wawasankha kuti akhale cholowa chake.+

  • Salimo 37:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Chifukwa anthu oipa adzaphedwa,+

      Koma amene akuyembekezera Yehova adzalandira dziko lapansi.+

  • Salimo 37:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Onani munthu wosalakwa,*

      Ndipo yangʼanitsitsani munthu wolungama,+

      Chifukwa tsogolo la munthu ameneyo lidzakhala lamtendere.+

  • Salimo 146:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Wosangalala ndi munthu amene amathandizidwa ndi Mulungu wa Yakobo,+

      Amene chiyembekezo chake chili mwa Yehova Mulungu wake,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena