Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 25:12, 13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ngati munthu amaopa Yehova,+

      Iye adzamulangiza njira imene akuyenera kusankha.+

      נ [Nun]

      13 Moyo wake udzasangalala ndi zinthu zabwino,+

      Ndipo mbadwa* zake zidzatenga dziko lapansi kuti likhale lawo.+

  • Salimo 37:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Olungama adzalandira dziko lapansi,+

      Ndipo adzakhala mmenemo mpaka kalekale.+

  • Mateyu 5:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Osangalala ndi anthu ofatsa+ chifukwa adzalandira dziko lapansi.+

  • 2 Petulo 2:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Zimenezi zikusonyeza kuti Yehova* amadziwa kupulumutsa anthu odzipereka kwa iye akakhala pa mayesero.+ Koma anthu osalungama amawasunga kuti adzawawononge pa tsiku lopereka chiweruzo,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena