Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 37:23, 24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Yehova akasangalala ndi njira za munthu+

      Amamusonyeza zoyenera kuchita pa moyo wake.+

      24 Ngakhale atapunthwa, sadzagweratu,+

      Chifukwa Yehova wamugwira dzanja kuti amuthandize.*+

  • Salimo 94:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Pamene ndinanena kuti: “Phazi langa likuterereka,”

      Chikondi chanu chokhulupirika, inu Yehova, chinapitiriza kundithandiza.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena