Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 19:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Munthu amakhala ndi mapulani ambiri mumtima mwake,

      Koma zolinga za Yehova nʼzimene zidzakwaniritsidwe.+

  • Yesaya 46:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kutatsala nthawi yaitali, ndimaneneratu zimene zidzachitike,

      Ndipo kale kwambiri ndinaneneratu zinthu zimene zidzachitike mʼtsogolo.+

      Ine ndimanena kuti, ‘Zolinga zanga zidzachitikadi,+

      Ndipo ndidzachita chilichonse chimene ndikufuna.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena