Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 135:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Yehova amachita chilichonse chimene wafuna+

      Kumwamba, padziko lapansi, mʼnyanja komanso mʼmalo onse ozama.

  • Yesaya 55:10, 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mofanana ndi mvula komanso sinowo* zimene zimagwa kuchokera kumwamba

      Ndipo sizibwerera kumeneko mpaka zitanyowetsa kwambiri nthaka nʼkuchititsa kuti mbewu zimere ndi kubereka zipatso,

      Nʼkupereka mbewu kuti anthu adzale komanso chakudya kuti adye,

      11 Ndi mmenenso adzakhalire mawu otuluka pakamwa panga.+

      Sadzabwerera kwa ine popanda kukwaniritsa cholinga chake,+

      Koma adzachitadi chilichonse chimene ine ndikufuna,+

      Ndipo zimene ndinawatumizira kuti achite zidzachitikadi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena