-
Mika 4:3Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
3 Mulungu adzaweruza mitundu yambiri ya anthu,+
Ndipo adzakonza zinthu zolakwika zokhudza anthu ochokera mʼmitundu yamphamvu yakutali.
Iwo adzasula malupanga awo kuti akhale makasu a pulawo,
Ndiponso mikondo yawo kuti ikhale zida zosadzira mitengo.+
Mtundu wa anthu sudzanyamula lupanga kuti umenyane ndi mtundu unzake,
Ndipo anthuwo sadzaphunziranso nkhondo.+
-