Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 6:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Ndikomereni mtima,* inu Yehova, chifukwa ndayamba kufooka.

      Ndichiritseni, inu Yehova,+ chifukwa mafupa anga akunjenjemera.

  • Salimo 38:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Thupi langa lonse likudwala* chifukwa cha mkwiyo wanu.

      Mʼmafupa anga mulibe mtendere chifukwa cha tchimo langa.+

  • Yesaya 57:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Chifukwa Wapamwamba ndi Wokwezeka,

      Amene adzakhalepo mpaka kalekale+ ndiponso dzina lake ndi loyera,+ wanena kuti:

      “Ine ndimakhala pamalo apamwamba komanso oyera,+

      Koma ndimakhalanso ndi anthu opsinjika ndiponso amene ali ndi mtima wodzichepetsa,

      Kuti nditsitsimutse mtima wa anthu onyozeka

      Ndiponso kuti nditsitsimutse mtima wa anthu opsinjika.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena