Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 37:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Koma anthu ofatsa adzalandira dziko lapansi,+

      Ndipo adzasangalala ndi mtendere wochuluka.+

  • Salimo 138:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Ngakhale kuti Yehova ali pamwamba, amaona wodzichepetsa,+

      Koma wonyada samuyandikira.+

  • Yesaya 57:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Chifukwa Wapamwamba ndi Wokwezeka,

      Amene adzakhalepo mpaka kalekale+ ndiponso dzina lake ndi loyera,+ wanena kuti:

      “Ine ndimakhala pamalo apamwamba komanso oyera,+

      Koma ndimakhalanso ndi anthu opsinjika ndiponso amene ali ndi mtima wodzichepetsa,

      Kuti nditsitsimutse mtima wa anthu onyozeka

      Ndiponso kuti nditsitsimutse mtima wa anthu opsinjika.+

  • Yakobo 4:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Komabe, kukoma mtima kwakukulu kumene Mulungu amapereka kumaposa khalidwe limeneli. Nʼchifukwa chake lemba limati: “Mulungu amatsutsa odzikuza,+ koma odzichepetsa amawasonyeza kukoma mtima kwake kwakukulu.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena