Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 72:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Mʼmasiku a ulamuliro wake, wolungama zinthu zidzamuyendera bwino,*+

      Ndipo padzakhala mtendere wochuluka+ kwa nthawi yonse imene mwezi udzakhalepo.

  • Salimo 119:165
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 165 Anthu amene amakonda chilamulo chanu amakhala ndi mtendere wochuluka,+

      Palibe chimene chingawakhumudwitse.*

  • Yesaya 48:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Zingakhale bwino kwambiri mutamvera malamulo anga!+

      Mukatero mtendere wanu udzakhala ngati mtsinje+

      Ndipo chilungamo chanu chidzakhala ngati mafunde a mʼnyanja.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena