Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 33:18, 19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Taonani! Diso la Yehova limayangʼana anthu amene amamuopa,+

      Amene amayembekezera chikondi chake chokhulupirika,

      19 Kuti awapulumutse ku imfa,

      Komanso kuwathandiza kuti akhale ndi moyo pa nthawi ya njala.+

  • Salimo 37:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Ndinali mwana ndipo tsopano ndakula,

      Koma sindinaonepo munthu aliyense wolungama atasiyidwa,+

      Kapena ana ake akupemphapempha chakudya.+

  • Mateyu 6:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Choncho nthawi zonse muziika Ufumu ndi mfundo zolungama za Mulungu pamalo oyamba pa moyo wanu, ndipo iye adzakupatsani zinthu zina zonsezi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena