Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 24:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Mukaiwala mtolo wa tirigu pokolola mʼmunda mwanu, musamabwerere kukatenga mtolowo. Muzisiyira mlendo wokhala mʼdziko lanu, mwana wamasiye ndi mkazi wamasiye.+ Muzichita zimenezi kuti Yehova Mulungu wanu akudalitseni pa chilichonse chimene mukuchita.+

  • Salimo 145:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Zamoyo zonse zimayangʼana kwa inu mwachiyembekezo.

      Mumazipatsa chakudya pa nyengo yake.+

  • Miyambo 10:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Yehova sadzachititsa kuti munthu wolungama akhale ndi njala,+

      Koma anthu oipa sadzawapatsa zimene amalakalaka.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena