Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 16:6, 7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Pamene iwo ankalowa, Samueli anaona Eliyabu+ ndipo anati: “Sindikukayikira, Yehova wasankha ameneyu.”* 7 Koma Yehova anauza Samueli kuti: “Usaganizire mmene akuonekera komanso kutalika kwake+ chifukwa ine ndamukana ameneyu. Chifukwatu mmene munthu amaonera si mmene Mulungu amaonera. Munthu amaona zooneka ndi maso, koma Yehova amaona mumtima.”+

  • Miyambo 24:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ukanena kuti: “Ifetu zimenezi sitimazidziwa,”

      Kodi amene amafufuza mitima sazindikira zimene zili mʼmaganizo mwako?+

      Ndithudi, amene amakuyangʼanitsitsa adzadziwa

      Ndipo adzabwezera munthu aliyense mogwirizana ndi zochita zake.+

  • Yeremiya 17:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ine Yehova ndimafufuza mtima,+

      Ndimafufuza maganizo a mkati mwa mtima wa munthu,*

      Kuti munthu aliyense ndimuchitire zinthu mogwirizana ndi zochita zake,

      Komanso mogwirizana ndi zipatso za ntchito zake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena