Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 37:25, 26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Ndinali mwana ndipo tsopano ndakula,

      Koma sindinaonepo munthu aliyense wolungama atasiyidwa,+

      Kapena ana ake akupemphapempha chakudya.+

      26 Nthawi zonse amakongoza ena zinthu zake mokoma mtima,+

      Ndipo ana ake adzalandira madalitso.

  • Salimo 112:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Iye wagawira ena mowolowa manja, wapereka kwa anthu osauka.+

      צ [Tsade]

      Chilungamo chake chidzakhalapo mpaka kalekale.+

      ק [Qoph]

      Mphamvu zake zidzawonjezeka* chifukwa cha ulemerero.

  • Luka 6:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Aliyense amene wakupempha kanthu mupatse,+ ndipo amene wakulanda zinthu usamuumirize kuti abweze.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena