Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mlaliki 2:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Palibe chabwino kwa munthu kuposa kuti adye, amwe ndi kusangalala chifukwa choti wagwira ntchito mwakhama.+ Ndinazindikira kuti zimenezinso nʼzochokera mʼdzanja la Mulungu woona,+

  • Mlaliki 3:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Ndinaona kuti palibe chabwino kuposa kuti munthu asangalale ndi ntchito yake+ chifukwa imeneyo ndi mphoto yake.* Nanga ndi ndani amene angamuchititse kuti aone zimene zidzachitike iye atafa.+

  • Yesaya 65:21, 22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Iwo adzamanga nyumba nʼkumakhalamo,+

      Ndipo adzadzala minda ya mpesa nʼkudya zipatso zake.+

      22 Sadzamanga nyumba kuti wina azikhalamo,

      Kapena kudzala kuti ena adye.

      Chifukwa masiku a anthu anga adzakhala ngati masiku a mtengo,+

      Ndipo anthu anga osankhidwa adzasangalala mokwanira ndi ntchito ya manja awo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena