Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 6:9, 10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Iye anamuuza kuti, “Pita ukauze anthu awa kuti:

      ‘Mudzamva mobwerezabwereza

      Koma simudzamvetsetsa.

      Mudzaona mobwerezabwereza,

      Koma simudzazindikira chilichonse.’+

      10 Uchititse anthu awa kuumitsa mtima wawo,+

      Uchititse makutu awo kuti asamamve,+

      Ndipo umate maso awo,

      Kuti asamaone ndi maso awowo,

      Ndiponso kuti asamamve ndi makutu awo,

      Nʼcholinga choti mtima wawo usamvetse zinthu

      Komanso kuti asabwerere nʼkuchiritsidwa.”

  • Yesaya 42:18, 19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Inu amene muli ndi vuto losamva, mvetserani.

      Inu amene muli ndi vuto losaona, yangʼanani kuti muone.+

      19 Kodi pali winanso amene ali ndi vuto losaona ngati mtumiki wanga,

      Amene ali ndi vuto losamva ngati munthu amene ndamutuma kukapereka uthenga?

      Kodi ndi ndani amene ali ndi vuto losaona ngati munthu amene wapatsidwa mphoto,

      Amene saona ngakhale pangʼono ngati mtumiki wa Yehova?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena