-
Yesaya 42:18, 19Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
18 Inu amene muli ndi vuto losamva, mvetserani.
Inu amene muli ndi vuto losaona, yangʼanani kuti muone.+
19 Kodi pali winanso amene ali ndi vuto losaona ngati mtumiki wanga,
Amene ali ndi vuto losamva ngati munthu amene ndamutuma kukapereka uthenga?
Kodi ndi ndani amene ali ndi vuto losaona ngati munthu amene wapatsidwa mphoto,
Amene saona ngakhale pangʼono ngati mtumiki wa Yehova?+
-