Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 78:69
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 69 Anachititsa kuti malo ake opatulika akhalepo mpaka kalekale ngati kumwamba,*+

      Ngati dziko lapansi limene analikhazikitsa mpaka kalekale.+

  • Salimo 104:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Iye wakhazikitsa dziko lapansi pamaziko ake.+

      Silidzasunthidwa pamalo ake* mpaka kalekale.+

  • Salimo 119:90
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 90 Kukhulupirika kwanu kudzakhalapobe ku mibadwo yonse.+

      Mwakhazikitsa mwamphamvu dziko lapansi, kuti lipitirizebe kukhalapo.+

  • Miyambo 3:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Yehova anayala maziko a dziko lapansi mwanzeru.+

      Anakhazikitsa kumwamba mozindikira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena