Numeri 23:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Mulungu sali ngati munthu amene amanena mabodza,+Sali ngati mwana wa munthu amene amasintha maganizo.*+ Akanena kanthu, kodi angalephere kuchita? Akalankhula, kodi angalephere kukwaniritsa?+ Yobu 23:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Akatsimikiza kuti achite zinthu, ndi ndani angamuletse?+ Akafuna kuchita chinthu, amachitadi.+
19 Mulungu sali ngati munthu amene amanena mabodza,+Sali ngati mwana wa munthu amene amasintha maganizo.*+ Akanena kanthu, kodi angalephere kuchita? Akalankhula, kodi angalephere kukwaniritsa?+