Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 31:10, 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Inu mitundu ya anthu, imvani mawu a Yehova,

      Ndipo mulengeze mawuwo kuzilumba zakutali kuti:+

      “Amene anabalalitsa Aisiraeli ndi amene adzawasonkhanitse.

      Adzawayangʼanira ngati mmene mʼbusa amachitira ndi nkhosa zake.+

      11 Chifukwa Yehova adzawombola Yakobo+

      Ndipo adzamupulumutsa mʼmanja mwa munthu wamphamvu kuposa iyeyo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena