Numeri 14:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 ‘Yehova ndi wosakwiya msanga, ndiponso wachikondi chokhulupirika chochuluka.*+ Amakhululukira zolakwa ndi machimo, koma sadzalekerera wolakwa osamupatsa chilango. Amalanga ana, zidzukulu ndi ana a zidzukuluzo chifukwa cha zolakwa za abambo awo.’+ Salimo 103:12, 13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Mofanana ndi mmene kotulukira dzuwa kwatalikirana ndi kolowera dzuwa,Mulungu waikanso zolakwa zathu kutali ndi ife.+ 13 Mofanana ndi bambo amene amasonyeza chifundo kwa ana ake,Yehova wasonyezanso chifundo kwa anthu amene amamuopa.+ Yesaya 43:25 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 25 Ineyo ndi amene ndikufafaniza zolakwa zako*+ chifukwa cha dzina langa,+Ndipo machimo ako sindidzawakumbukira.+
18 ‘Yehova ndi wosakwiya msanga, ndiponso wachikondi chokhulupirika chochuluka.*+ Amakhululukira zolakwa ndi machimo, koma sadzalekerera wolakwa osamupatsa chilango. Amalanga ana, zidzukulu ndi ana a zidzukuluzo chifukwa cha zolakwa za abambo awo.’+
12 Mofanana ndi mmene kotulukira dzuwa kwatalikirana ndi kolowera dzuwa,Mulungu waikanso zolakwa zathu kutali ndi ife.+ 13 Mofanana ndi bambo amene amasonyeza chifundo kwa ana ake,Yehova wasonyezanso chifundo kwa anthu amene amamuopa.+
25 Ineyo ndi amene ndikufafaniza zolakwa zako*+ chifukwa cha dzina langa,+Ndipo machimo ako sindidzawakumbukira.+