Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 25:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Musakumbukire machimo amene ndinachita ndili mnyamata komanso zolakwa zanga.

      Mundikumbukire chifukwa cha ubwino wanu, inu Yehova,+

      Mogwirizana ndi chikondi chanu chokhulupirika.+

  • Salimo 79:8, 9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Musatiimbe mlandu chifukwa cha zolakwa za makolo athu.+

      Tisonyezeni chifundo chanu mofulumira,+

      Chifukwa zativuta kwambiri.

       9 Tithandizeni inu Mulungu amene mumatipulumutsa,+

      Chifukwa cha dzina lanu laulemerero.

      Tipulumutseni komanso mutikhululukire* machimo athu chifukwa cha dzina lanu.+

  • Ezekieli 20:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Koma ndinachitapo kanthu chifukwa cha dzina langa kuti lisadetsedwe pamaso pa anthu a mitundu ina kumene ankakhalako.+ Chifukwa ndinachititsa kuti iwo* andidziwe pamaso pa anthu a mitundu inawo pamene ndinawatulutsa* mʼdziko la Iguputo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena