Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 35:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Chipululu ndi dziko louma zidzasangalala,+

      Dera lachipululu lidzakondwa ndipo lidzachita maluwa ambiri.*+

       2 Deralo lidzachitadi maluwa.+

      Lidzasangalala ndipo lidzafuula chifukwa cha chisangalalo.

      Lidzapatsidwa ulemerero wa Lebanoni,+

      Kukongola kwa Karimeli+ ndiponso kwa Sharoni.+

      Anthu adzaona ulemerero wa Yehova ndi kukongola kwa Mulungu wathu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena