-
Ezekieli 11:21Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
21 “‘“Koma amene atsimikiza mumtima mwawo kuti apitirize kutsatira mafano awo onyansa komanso kuchita zinthu zonyansa, ndidzawabwezera mogwirizana ndi zochita zawo,” akutero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.’”
-