Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 2:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Mitunduyo udzaiphwanya ndi ndodo yachifumu yachitsulo,+

      Ndipo udzaiswa ngati chiwiya chadothi.”+

  • Salimo 110:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Yehova adzatambasula ndodo yako yachifumu kuti ulamulirenso madera ena osati mu Ziyoni mokha. Iye adzanena kuti:

      “Pita pakati pa adani ako ndipo ukawagonjetse.”+

  • Chivumbulutso 19:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndinaona kumwamba kutatseguka, kenako ndinaona hatchi yoyera.+ Amene anakwera pahatchiyo dzina lake linali lakuti Wokhulupirika+ ndi Woona.+ Iye amaweruza molungama ndipo akumenya nkhondo mwachilungamo.+

  • Chivumbulutso 19:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Mʼkamwa mwake munkatuluka lupanga lalitali+ lakuthwa, loti aphere mitundu ya anthu ndipo adzawakusa ndi ndodo yachitsulo.+ Komanso iye ankapondaponda muchopondera mphesa cha mkwiyo waukulu wa Mulungu Wamphamvuyonse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena