Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 43:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Yehova, Wokuwombolani,+ Woyera wa Isiraeli,+ wanena kuti:

      “Chifukwa cha inu, ndidzatumiza asilikali ku Babulo ndipo adzagwetsa zotsekera mʼmageti,+

      Komanso Akasidi adzalira chifukwa chopanikizika, ali mʼsitima zawo zapamadzi.+

  • Yeremiya 50:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Yehova watsegula nyumba yake yosungiramo zida,

      Ndipo akutulutsamo zida zimene amagwiritsa ntchito posonyeza mkwiyo wake.+

      Chifukwa Yehova wa magulu ankhondo akumwamba, Ambuye Wamkulu Koposa, ali ndi ntchito yoti achite

      Mʼdziko la Akasidi.

  • Yeremiya 51:56
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 56 Wowononga adzafikira Babulo.+

      Asilikali ake adzagwidwa,+

      Mauta awo adzathyoledwa,

      Chifukwa Yehova ndi Mulungu amene amapereka chilango choyenera.+

      Iye adzabwezera ndithu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena