Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 119:165
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 165 Anthu amene amakonda chilamulo chanu amakhala ndi mtendere wochuluka,+

      Palibe chimene chingawakhumudwitse.*

  • Yesaya 55:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Chifukwa mudzapita mukusangalala,+

      Ndipo adzakubweretsani kwanu mwamtendere.+

      Mukadzafika, mapiri ndi zitunda zidzafuula mosangalala,+

      Ndipo mitengo yonse yakutchire idzawomba mʼmanja.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena