Yesaya 51:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Anthu owomboledwa a Yehova adzabwerera.+ Adzabwera ku Ziyoni akufuula mosangalala,+Ndipo pamutu pawo padzakhala chisangalalo mpaka kalekale.+ Iwo adzapeza chisangalalo ndi chimwemwe,Ndipo chisoni komanso kulira zidzachoka.+ Yeremiya 31:11, 12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Chifukwa Yehova adzawombola Yakobo+Ndipo adzamupulumutsa mʼmanja mwa munthu wamphamvu kuposa iyeyo.+ 12 Iwo adzabwera nʼkufuula mosangalala pamwamba pa phiri la Ziyoni.+Nkhope zawo zidzawala chifukwa cha ubwino wa* Yehova.Chifukwa cha mbewu, vinyo watsopano+ ndi mafuta,Ndiponso chifukwa cha ana a nkhosa ndi ana a ngʼombe.+ Iwo adzakhala ngati dimba lothiriridwa bwino+Ndipo sadzakhalanso ofooka.”+
11 Anthu owomboledwa a Yehova adzabwerera.+ Adzabwera ku Ziyoni akufuula mosangalala,+Ndipo pamutu pawo padzakhala chisangalalo mpaka kalekale.+ Iwo adzapeza chisangalalo ndi chimwemwe,Ndipo chisoni komanso kulira zidzachoka.+
11 Chifukwa Yehova adzawombola Yakobo+Ndipo adzamupulumutsa mʼmanja mwa munthu wamphamvu kuposa iyeyo.+ 12 Iwo adzabwera nʼkufuula mosangalala pamwamba pa phiri la Ziyoni.+Nkhope zawo zidzawala chifukwa cha ubwino wa* Yehova.Chifukwa cha mbewu, vinyo watsopano+ ndi mafuta,Ndiponso chifukwa cha ana a nkhosa ndi ana a ngʼombe.+ Iwo adzakhala ngati dimba lothiriridwa bwino+Ndipo sadzakhalanso ofooka.”+