Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 17:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Koma mfumu ya Asuri inamva kuti Hoshiya akuikonzera chiwembu, chifukwa anatumiza anthu kwa So mfumu ya Iguputo+ ndiponso sanapereke msonkho kwa mfumu ya Asuri ngati mmene ankachitira zaka zamʼmbuyo. Choncho mfumu ya Asuri inamʼmanga nʼkumutsekera mʼndende.

  • Yesaya 30:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Iwo amapita ku Iguputo+ asanandifunse,+

      Kuti akapeze chitetezo kwa Farao*

      Ndiponso kuti akabisale mumthunzi wa Iguputo.

  • Yesaya 30:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Chifukwa thandizo lochokera ku Iguputo ndi losathandiza ngakhale pangʼono.+

      Choncho iye ndamutchula kuti: “Rahabi+ amene amangokhala osachita chilichonse.”

  • Yeremiya 37:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 “Yehova Mulungu wa Isiraeli wanena kuti, ‘Mfumu ya Yuda imene yakutumani kudzafunsira kwa ine mukaiuze kuti: “Taonani! Asilikali a Farao amene akubwera kudzakuthandizani adzabwerera kwawo ku Iguputo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena