-
Salimo 74:8Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
8 Iwo limodzi ndi ana awo ananena mumtima mwawo kuti:
“Malo onse amene anthu amalambirirako Mulungu mʼdzikoli, ayenera kutenthedwa.”
-
-
Ezekieli 24:21Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
21 ‘Uza nyumba ya Isiraeli kuti: “Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti, ‘Ndatsala pangʼono kudetsa malo anga opatulika,+ chinthu chimene mumachinyadira kwambiri, chinthu chimene mumachikonda komanso chapamtima panu. Ana anu aamuna ndi aakazi amene munawasiya mumzindawo adzaphedwa ndi lupanga.+
-