Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 30:10, 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti: ‘Ndidzawononga magulu a anthu a ku Iguputo pogwiritsa ntchito dzanja la Nebukadinezara,* mfumu ya Babulo.+ 11 Mfumuyo ndi asilikali ake, omwe ndi ankhanza kwambiri pa mayiko onse,+ adzabweretsedwa kuti adzawononge dzikolo. Iwo adzasolola malupanga awo nʼkuukira Iguputo ndipo adzadzaza dzikolo ndi anthu ophedwa.+

  • Habakuku 1:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Ine ndikubweretsa Akasidi,+

      Mtundu wankhanza ndiponso waphuma.

      Umene umathamanga mʼmadera ambiri apadziko lapansi,

      Kukalanda nyumba zimene si zawo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena