-
Danieli 9:22Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
22 Iye anandithandiza kuti ndimvetse, ndipo anandiuza kuti:
“Iwe Danieli, tsopano ndabwera kuti ndikupatse nzeru ndi kukuthandiza kumvetsa zinthu zonsezi.
-