Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 22:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Mulungu wanga, Mulungu wanga, mwandisiyiranji ine?+

      Nʼchifukwa chiyani mukuchedwa kundipulumutsa?

      Nʼchifukwa chiyani simukumva kubuula kwanga?+

  • Salimo 74:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Inu Mulungu, kodi mdani adzapitiriza kunyoza mpaka liti?+

      Kodi mdani adzachitira mwano dzina lanu mpaka kalekale?+

  • Chivumbulutso 6:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Iwo anafuula ndi mawu okweza akuti: “Mudzalekerera mpaka liti, inu Ambuye Wamkulu Koposa, Mulungu woyera ndi woona,+ osaweruza ndi kubwezera okhala padziko lapansi chifukwa cha magazi athu?”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena