Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 3:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pita, ndipo ukalengeze mawu awa kumpoto:+

      ‘Yehova wanena kuti:+ “Bwerera Isiraeli wopanduka iwe. Sindidzakuyangʼana mokwiya+ chifukwa ndine wokhulupirika,” akutero Yehova. “Sindidzakhala wokwiya mpaka kalekale.

  • Zekariya 1:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Uwauze kuti, ‘Yehova wa magulu ankhondo akumwamba wanena kuti: “Bwererani kwa ine,” watero Yehova wa magulu ankhondo akumwamba, “ndipo ine ndidzabwerera kwa inu,”+ akutero Yehova wa magulu ankhondo akumwamba.’”

  • Yakobo 4:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Yandikirani Mulungu ndipo iyenso adzakuyandikirani.+ Yeretsani manja anu ochimwa inu,+ ndipo yeretsani mitima yanu+ okayikakayika inu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena