Maliko 3:14, 15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Ndiyeno anasankha gulu la anthu 12, amenenso anawapatsa dzina lakuti atumwi, kuti aziyenda naye nthawi zonse komanso kuti aziwatuma kukalalikira 15 nʼkuwapatsa mphamvu zoti azitulutsa ziwanda.+ Maliko 6:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Kenako anaitana ophunzira ake 12 aja nʼkuyamba kuwatumiza awiriawiri+ ndipo anawapatsa mphamvu kuti azitha kutulutsa mizimu yonyansa.+ Luka 9:1, 2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Kenako Yesu anasonkhanitsa atumwi 12 aja nʼkuwapatsa mphamvu ndi ulamuliro pa ziwanda zonse+ komanso kuti azitha kuchiritsa matenda.+ 2 Ndiyeno anawatumiza kuti azikalalikira za Ufumu wa Mulungu ndiponso kuchiritsa anthu.
14 Ndiyeno anasankha gulu la anthu 12, amenenso anawapatsa dzina lakuti atumwi, kuti aziyenda naye nthawi zonse komanso kuti aziwatuma kukalalikira 15 nʼkuwapatsa mphamvu zoti azitulutsa ziwanda.+
7 Kenako anaitana ophunzira ake 12 aja nʼkuyamba kuwatumiza awiriawiri+ ndipo anawapatsa mphamvu kuti azitha kutulutsa mizimu yonyansa.+
9 Kenako Yesu anasonkhanitsa atumwi 12 aja nʼkuwapatsa mphamvu ndi ulamuliro pa ziwanda zonse+ komanso kuti azitha kuchiritsa matenda.+ 2 Ndiyeno anawatumiza kuti azikalalikira za Ufumu wa Mulungu ndiponso kuchiritsa anthu.