Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 7:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Palibe chilichonse chochokera kunja kwa munthu nʼkulowa mʼthupi mwake chimene chingaipitse munthu. Koma zinthu zimene zimatuluka mwa munthu ndi zimene zimaipitsa munthu.”+

  • Aefeso 4:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Mawu owola asamatuluke pakamwa panu,+ koma pazituluka mawu abwino okha kuti alimbikitse ena pakafunika kutero, kuti athandize anthu amene akumvetsera.+

  • Yakobo 3:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Lilimenso ndi moto.+ Pa ziwalo zonse za thupi lathu, lilime ndi lodzaza ndi zinthu zosalungama chifukwa limadetsa thupi lonse+ komanso limayatsa moyo wonse wa munthu* ndipo lili ndi moto wa Gehena.*

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena