Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 55:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Munthu woipa asiye njira yake+

      Ndipo wopweteka anzake asiye maganizo ake.

      Iye abwerere kwa Yehova ndipo adzamuchitira chifundo.+

      Abwerere kwa Mulungu wathu, chifukwa adzamukhululukira ndi mtima wonse.+

  • Mateyu 6:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mutikhululukire zolakwa* zathu chifukwa ifenso takhululukira amene atilakwira.*+

  • Mateyu 7:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Choncho zinthu zonse zimene mukufuna kuti anthu akuchitireni, inunso muwachitire zomwezo.+ Zimenezi ndi zomwe Chilamulo chimafuna komanso zimene aneneri analemba.+

  • Yakobo 2:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Chifukwa munthu amene sasonyeza chifundo adzaweruzidwa mopanda chifundo.+ Chifundo nʼchachikulu kuposa chiweruzo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena