Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 26:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Choncho atapita patsogolo pangʼono, anagwada mpaka nkhope yake pansi ndipo anapemphera kuti:+ “Atate wanga, ngati nʼkotheka lolani kuti kapu iyi+ indipitirire. Koma osati mwa kufuna kwanga, koma mwa kufuna kwanu.”+

  • Maliko 10:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Koma Yesu anawauza kuti: “Simukudziwa chimene mukupempha. Kodi mungamwe zimene ine ndikumwa kapena kubatizidwa ubatizo umene ine ndikubatizidwa?”+

  • Maliko 14:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Kenako anati: “Abba,* Atate,+ zinthu zonse nʼzotheka kwa inu. Ndichotsereni kapu iyi. Komatu osati mwa kufuna kwanga, koma mwa kufuna kwanu.”+

  • Yohane 18:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Koma Yesu anauza Petulo kuti: “Bwezera lupangalo mʼchimake.+ Kodi sindiyenera kumwa zamʼkapu imene Atate wandipatsa?”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena