Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 26:57
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 57 Anthu amene anagwira Yesu aja anapita naye kwa Kayafa+ mkulu wa ansembe, kumene alembi ndi akulu anali atasonkhana.+

  • Luka 22:54, 55
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 54 Zitatero anamugwira nʼkumutenga+ ndipo anakamulowetsa mʼnyumba ya mkulu wa ansembe. Koma Petulo ankawatsatira chapatali.+ 55 Atasonkha moto mkati mwa bwalo nʼkukhala pansi onse pamodzi, Petulo nayenso anakhala nawo pamenepo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena