Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Luka 3:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Yohane anayankha onsewo kuti: “Ine ndikukubatizani ndi madzi. Koma wina wamphamvu kuposa ine akubwera, amene ine sindili woyenera kumasula zingwe za nsapato zake.+ Iyeyu adzakubatizani ndi mzimu woyera komanso moto.+

  • Yohane 1:26, 27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Yohane anawayankha kuti: “Ine ndimabatiza mʼmadzi. Pakati panu paimirira wina amene inu simukumudziwa. 27 Iye ndi amene akubwera mʼmbuyo mwangamu ndipo ine si woyenera kumasula zingwe za nsapato zake.”+

  • Machitidwe 13:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Koma pamene Yohane ankamaliza utumiki wake, ankanena kuti, ‘Kodi mukuganiza kuti ndine ndani? Amene mukumuganizirayo si ine ayi. Koma wina akubwera pambuyo panga, amene ine si woyenera kumasula nsapato zake.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena