Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 7:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 “Siyani kuweruza ena+ kuti inunso musaweruzidwe, 2 chifukwa mmene mumaweruzira ena inunso adzakuweruzani choncho.+ Ndipo muyezo umene mukuyezera ena iwonso adzakuyezerani womwewo.+

  • Aroma 14:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Nanga nʼchifukwa chiyani umaweruza mʼbale wako?+ Kapenanso nʼchifukwa chiyani umanyoza mʼbale wako? Popeza tonse tidzaima patsogolo pa mpando woweruzira wa Mulungu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena