Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yohane 14:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Sindilankhula nanu zambiri chifukwa wolamulira wa dziko+ akubwera ndipo alibe mphamvu pa ine.+

  • Yohane 16:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Pomaliza adzapereka umboni wonena za chiweruzo, chifukwa wolamulira wa dziko lino waweruzidwa.+

  • Machitidwe 26:17, 18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ndipo ndidzakupulumutsa kwa anthu awa komanso kwa anthu a mitundu ina kumene ndikukutumiza+ 18 kuti ukatsegule maso awo,+ kuwachotsa mumdima+ nʼkuwapititsa kowala+ ndiponso kuwachotsa mʼmanja mwa Satana+ nʼkuwapititsa kwa Mulungu. Ukachite zimenezi kuti machimo awo akhululukidwe+ nʼkulandira cholowa pamodzi ndi oyeretsedwa chifukwa chondikhulupirira.’

  • 2 Akorinto 4:3, 4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ngati uthenga wabwino umene tikulalikira uli wophimbika, ndi wophimbika kwa anthu amene akupita kukawonongedwa, 4 anthu osakhulupirira amene mulungu wa nthawi* ino+ wachititsa khungu maganizo awo+ kuti asaone kuwala+ kwa uthenga wabwino waulemerero wonena za Khristu, yemwe ndi chifaniziro cha Mulungu.+

  • Aefeso 2:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Kuwonjezera pamenepo, Mulungu anapangitsa kuti mukhale amoyo ngakhale kuti munali akufa chifukwa cha zolakwa zanu komanso machimo anu.+ 2 Pa nthawi ina munkachita zimenezi mogwirizana ndi nthawi* za mʼdzikoli,+ pomvera wolamulira wa mpweya+ umene umalamulira zochita za anthu. Mpweya umenewu, kapena kuti kaganizidwe+ kameneka, tsopano kakugwira ntchito mwa ana osamvera.

  • 1 Yohane 5:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Tikudziwa kuti ndife anthu a Mulungu, koma dziko lonse lili mʼmanja mwa woipayo.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena