Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 12:4, 5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Choncho Abulamu ananyamuka monga mmene Yehova anamuuzira, ndipo Loti ananyamuka naye limodzi. Pamene ankachoka ku Harana, Abulamu anali ndi zaka 75.+ 5 Abulamu anatenga mkazi wake Sarai,+ Loti mwana wa mʼbale+ wake ndi chuma chawo chonse+ komanso akapolo awo onse amene anapeza kudziko la Harana. Iwo ananyamuka ulendo wopita kudziko la Kanani.+ Atafika ku Kanani,

  • Aheberi 11:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Chifukwa cha chikhulupiriro, Abulahamu+ ataitanidwa, anamvera nʼkupita kumalo amene ankayembekezera kuwalandira ngati cholowa. Iye anapitadi, ngakhale kuti sankadziwa kumene akupita.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena