Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 28:19, 20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Choncho pitani mukaphunzitse anthu a mitundu yonse kuti akhale ophunzira anga.+ Muziwabatiza+ mʼdzina la Atate, la Mwana ndi la mzimu woyera, 20 ndipo muziwaphunzitsa kuti azisunga zinthu zonse zimene ndinakulamulani.+ Ndipo dziwani kuti ine ndili limodzi ndi inu masiku onse mpaka mʼnyengo ya mapeto a nthawi* ino.”+

  • 2 Timoteyo 4:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Lalikira mawu.+ Uzilalikira modzipereka, pa nthawi yabwino ndi pa nthawi yovuta. Dzudzula,+ tsutsa, dandaulira, ndipo uzichita zimenezi ndi luso la kuphunzitsa+ ndiponso moleza mtima kwambiri.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena