Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 20:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Komatu sindinakubisireni chilichonse chothandiza ndipo sindinasiye kukuphunzitsani pagulu+ komanso kunyumba ndi nyumba.+

  • 1 Akorinto 11:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Zimene ndinamva kwa Ambuye nʼzimene inenso ndinakuphunzitsani, kuti Ambuye Yesu, usiku+ umene anaperekedwa anatenga mkate,

  • 2 Petulo 3:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Okondedwa, iyi tsopano ndi kalata yachiwiri imene ndikukulemberani, ndipo mofanana ndi yoyamba ija, ndikukulimbikitsani kuti muzigwiritsa ntchito bwino mphamvu zanu zoganiza pokukumbutsani zimene mukudziwa kale.+ 2 Ndikuchita zimenezi kuti mukumbukire mawu amene aneneri oyera ananena kalero komanso lamulo limene Ambuye ndi Mpulumutsi wathu anapereka kudzera mwa atumwi.*

  • 1 Yohane 3:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Lamulo limene anatipatsa ndi lakuti, tikhale ndi chikhulupiriro mʼdzina la Mwana wake Yesu Khristu+ ndiponso tizikondana,+ monga mmene iye anatilamulira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena