Mateyu 26:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 Akupitiriza kudya, Yesu anatenga mkate ndipo atayamika Mulungu, anaunyemanyema+ nʼkuupereka kwa ophunzira ake. Iye ananena kuti: “Eni, idyani. Mkate uwu ukuimira thupi langa.”+ Maliko 14:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Akupitiriza kudya, iye anatenga mkate nʼkuyamika Mulungu. Kenako anaunyemanyema nʼkuwapatsa ndipo anati: “Tengani, mkate uwu ukuimira thupi langa.”+ Aroma 7:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Abale anga, thupi la Khristu linakumasulani ku Chilamulo, kuti mukhale a winawake+ amene anaukitsidwa+ nʼcholinga choti tibale zipatso kwa Mulungu.+ 1 Akorinto 10:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Popeza pali mkate umodzi, ifeyo, ngakhale kuti tilipo ambiri, ndife thupi limodzi,+ chifukwa tonse tikudya nawo mkate umodziwo.
26 Akupitiriza kudya, Yesu anatenga mkate ndipo atayamika Mulungu, anaunyemanyema+ nʼkuupereka kwa ophunzira ake. Iye ananena kuti: “Eni, idyani. Mkate uwu ukuimira thupi langa.”+
22 Akupitiriza kudya, iye anatenga mkate nʼkuyamika Mulungu. Kenako anaunyemanyema nʼkuwapatsa ndipo anati: “Tengani, mkate uwu ukuimira thupi langa.”+
4 Abale anga, thupi la Khristu linakumasulani ku Chilamulo, kuti mukhale a winawake+ amene anaukitsidwa+ nʼcholinga choti tibale zipatso kwa Mulungu.+
17 Popeza pali mkate umodzi, ifeyo, ngakhale kuti tilipo ambiri, ndife thupi limodzi,+ chifukwa tonse tikudya nawo mkate umodziwo.