Deuteronomo 16:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Ndiyeno muzichitira Yehova Mulungu wanu Chikondwerero cha Masabata,+ popereka nsembe zaufulu zimene mungathe, mogwirizana ndi mmene Yehova Mulungu wanu wakudalitsirani.+ Deuteronomo 16:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Mphatso imene aliyense ayenera kubweretsa izikhala yogwirizana ndi madalitso amene Yehova Mulungu wanu wakupatsani.+ Miyambo 3:27, 28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 Usalephere kuchitira zabwino anthu amene ukuyenera kuwachitira* zabwinozo,+Ngati ungathe kuwathandiza.*+ 28 Mnzako usamuuze kuti, “Pita, ukabwerenso mawa ndipo ndidzakupatsa,” Ngati ungathe kumupatsa nthawi yomweyo.
10 Ndiyeno muzichitira Yehova Mulungu wanu Chikondwerero cha Masabata,+ popereka nsembe zaufulu zimene mungathe, mogwirizana ndi mmene Yehova Mulungu wanu wakudalitsirani.+
17 Mphatso imene aliyense ayenera kubweretsa izikhala yogwirizana ndi madalitso amene Yehova Mulungu wanu wakupatsani.+
27 Usalephere kuchitira zabwino anthu amene ukuyenera kuwachitira* zabwinozo,+Ngati ungathe kuwathandiza.*+ 28 Mnzako usamuuze kuti, “Pita, ukabwerenso mawa ndipo ndidzakupatsa,” Ngati ungathe kumupatsa nthawi yomweyo.