Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 34:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Mngelo wa Yehova amamanga msasa kuzungulira anthu onse amene amaopa Mulungu,+

      Ndipo amawapulumutsa.+

  • Salimo 91:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Chifukwa adzalamula angelo ake+ zokhudza iwe,

      Kuti akuteteze mʼnjira zako zonse.+

  • Machitidwe 5:18, 19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 nʼkugwira atumwiwo ndipo anawatsekera mʼndende.+ 19 Koma usiku, mngelo wa Yehova* anatsegula zitseko za ndendeyo nʼkuwatulutsa,+ ndipo anawauza kuti:

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena