Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 6:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Kenako Elisa anayamba kupemphera kuti: “Inu Yehova, chonde mutseguleni maso kuti aone.”+ Nthawi yomweyo Yehova anatsegula maso a mtumikiyo, moti anaona kuti dera lonse lamapiri kuzungulira Elisa+ linadzaza ndi mahatchi ndi magaleta ankhondo oyaka moto.+

  • Salimo 91:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Chifukwa adzalamula angelo ake+ zokhudza iwe,

      Kuti akuteteze mʼnjira zako zonse.+

  • Mateyu 18:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Samalani anthu inu kuti musanyoze mmodzi wa tianati, chifukwa ndikukutsimikizirani kuti angelo awo kumwamba amaona nkhope ya Atate wanga wakumwamba nthawi zonse.+

  • Aheberi 1:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ndiponso ponena za angelo, iye akuti: “Amachititsa kuti angelo ake akhale amphamvu* ndipo amachititsa atumiki ake+ kukhala ngati lawi la moto.”+

  • Aheberi 1:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Angelo onse ndi mizimu yotumikira ena.*+ Mulungu amawatumiza kuti akatumikire omwe iye adzawapulumutse.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena