Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 10:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Chidani nʼchimene chimayambitsa mikangano,

      Koma chikondi chimaphimba machimo onse.+

  • Miyambo 17:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Aliyense amene amakhululuka* zolakwa akufunafuna chikondi,+

      Koma amene amangokhalira kulankhula za nkhani inayake amalekanitsa mabwenzi apamtima.+

  • 1 Akorinto 13:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Chikondi+ nʼcholeza mtima+ ndiponso nʼchokoma mtima.+ Chikondi sichichita nsanje,+ sichidzitama, sichidzikuza,+

  • 1 Akorinto 13:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Chimakwirira zinthu zonse,+ chimakhulupirira zinthu zonse,+ chimayembekezera zinthu zonse+ komanso chimapirira zinthu zonse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena