Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 11:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Ngati wolungama padziko lapansi amapatsidwa mphoto,

      Ndiye kuli bwanji woipa ndi wochimwa?+

  • Mateyu 7:13, 14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Lowani pageti lalingʼono.+ Chifukwa msewu umene ukupita kuchiwonongeko ndi wotakasuka komanso geti lake ndi lalikulu ndipo anthu ambiri akudzera pageti limenelo. 14 Koma geti lolowera ku moyo ndi lalingʼono komanso msewu wake ndi wopanikiza ndipo amene akuupeza ndi ochepa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena